1 Pulumutseni Inu Mulungu,
2 Ine ndikumira mʼthope lozama
3 Ndafowoka ndikupempha chithandizo;
4 Iwo amene amadana nane popanda chifukwa
5 Mukudziwa uchitsiru wanga, Inu Mulungu,
6 Iwo amene amadalira Inu
7 Pakuti ndimapirira kunyozedwa chifukwa cha Inu,
8 Ndine mlendo kwa abale anga,
9 pakuti changu chochitira nyumba yanu chandiphetsa
10 Pamene ndikulira ndi kusala kudya,
11 pomwe ndavala chiguduli,
12 Iwo amene amakhala pa chipata amandinena,
13 Koma ndikupempha kwa Inu Ambuye,
14 Mundilanditse kuchoka mʼmatope,
15 Musalole kuti chigumula chindimeze,
16 Ndiyankheni Inu Yehova mwa ubwino wanu wa chikondi chanu;
17 Musabisire nkhope yanu mtumiki wanu,
18 Bwerani pafupi ndi kundilanditsa;
19 Inu mukudziwa momwe ndanyozedwera,
20 Mnyozo waswa mtima wanga
21 Iwo anayika ndulu mʼchakudya changa
22 Chakudya chomwe chayikidwa patsogolo pawo chikhale msampha;
23 Maso awo adetsedwe kotero kuti asaonenso
24 Khuthulirani ukali wanu pa iwo;
25 Malo awo akhale wopanda anthu
26 Pakuti iwo amazunza amene inu munamuvulaza
27 Awonjezereni kulakwa pa kulakwa kwawo,
28 Iwo afufutidwe mʼbuku la amoyo
29 Ndikumva zowawa ndi kuzunzika;
30 Ine ndidzatamanda dzina la Mulungu mʼnyimbo,
31 Izi zidzakondweretsa Yehova kupambana ngʼombe,
32 Wosauka adzaona ndipo adzasangalala,
33 Yehova amamvera anthu osowa
34 Kumwamba ndi dziko lapansi zitamanda Iye,
35 pakuti Mulungu adzapulumutsa Ziyoni
36 ana atumiki ake adzalitenga kukhala cholowa chawo,