Salmos 58

NYA

1 Kodi inu olamulira mumayankhuladi molungama?

2 Ayi, mʼmitima mwanu mumakonzekera zosalungama,

3 Ngakhale kuchokera tsiku lawo lobadwa oyipa amasochera;

4 Ululu wawo uli ngati ululu wa njoka,

5 Imene simva liwu la munthu wamatsenga,

6 Gululani mano mʼkamwa mwawo, Inu Mulungu,

7 Mulole kuti asowe ngati madzi oyenda

8 Akhale ngati nkhono imene imasungunuka pamene ikuyenda;

9 Miphika yanu isanagwire moto waminga ya mkandankhuku,

10 Olungama adzasangalala poona kubwezera chilango,

11 Ndipo anthu adzanena kuti,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado