1 Kodi inu olamulira mumayankhuladi molungama?
2 Ayi, mʼmitima mwanu mumakonzekera zosalungama,
3 Ngakhale kuchokera tsiku lawo lobadwa oyipa amasochera;
4 Ululu wawo uli ngati ululu wa njoka,
5 Imene simva liwu la munthu wamatsenga,
6 Gululani mano mʼkamwa mwawo, Inu Mulungu,
7 Mulole kuti asowe ngati madzi oyenda
8 Akhale ngati nkhono imene imasungunuka pamene ikuyenda;
9 Miphika yanu isanagwire moto waminga ya mkandankhuku,
10 Olungama adzasangalala poona kubwezera chilango,
11 Ndipo anthu adzanena kuti,