1 Mundichitire chifundo, Inu Mulungu mundichitire chifundo,
2 Ine ndikufuwulira kwa Mulungu Wammwambamwamba,
3 Mulungu amanditumizira kuchokera kumwamba ndi kundipulumutsa,
4 Ine ndili pakati pa mikango,
5 Mukwezekedwe Inu Mulungu, kuposa mayiko onse akumwamba;
6 Iwo anatchera mapazi anga ukonde
7 Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu
8 Dzuka moyo wanga!
9 Ndidzakutamandani Ambuye, pakati pa mitundu ya anthu,
10 Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kufikira ku mayiko akumwamba;
11 Mukwezekedwe Inu Mulungu kuposa mayiko akumwamba,