Salmos 57

NYA

1 Mundichitire chifundo, Inu Mulungu mundichitire chifundo,

2 Ine ndikufuwulira kwa Mulungu Wammwambamwamba,

3 Mulungu amanditumizira kuchokera kumwamba ndi kundipulumutsa,

4 Ine ndili pakati pa mikango,

5 Mukwezekedwe Inu Mulungu, kuposa mayiko onse akumwamba;

6 Iwo anatchera mapazi anga ukonde

7 Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu

8 Dzuka moyo wanga!

9 Ndidzakutamandani Ambuye, pakati pa mitundu ya anthu,

10 Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kufikira ku mayiko akumwamba;

11 Mukwezekedwe Inu Mulungu kuposa mayiko akumwamba,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado