Salmos 56

NYA

1 Mundichitire chifundo Inu Mulungu, pakuti anthu akundithamangitsa kwambiri;

2 Ondinyoza akundithamangitsa tsiku lonse,

3 Ndikachita mantha

4 Mwa Mulungu, amene mawu ake ine ndimatamanda,

5 Tsiku lonse amatembenuza mawu anga;

6 Iwo amakambirana, amandibisalira,

7 Musalole konse kuti athawe;

8 Mulembe za kulira kwanga,

9 Adani anga adzabwerera mʼmbuyo

10 Mwa Mulungu amene mawu ake ndimawatamanda,

11 mwa Mulungu ine ndimadalira ndipo sindidzachita mantha.

12 Ndiyenera kuchita zomwe ndinalumbira kwa Mulungu;

13 Pakuti mwawombola moyo wanga ku imfa

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado