1 Mvetserani pemphero langa, Inu Mulungu,
2 mverani ndipo mundiyankhe.
3 chifukwa cha mawu a adani anga,
4 Mtima wanga ukupweteka mʼkati mwanga;
5 Mantha ndi kunjenjemera zandizinga;
6 Ndinati, “Ndithu, ndikanakhala ndi mapiko ankhunda!
7 Ndikanathawira kutali
8 Ndikanathamangira kumalo anga a chitetezo;
9 Sokonezani maganizo a oyipa, Inu Ambuye, tsutsani mawu awo;
10 Usana ndi usiku iwo akuzungulirazungulira pa makoma ake;
11 Mphamvu zowononga zili pa ntchito mu mzinda;
12 Akanakhala mdani akundinyoza, ine
13 Koma iweyo mnzanga, mnzanga woyenda naye,
14 Mnzanga amene nthawi ina tinkasangalala
15 Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi;
16 Koma ine ndinafuwulira kwa Mulungu,
17 Madzulo, mmawa ndi masana
18 Iye amandiwombola ine osavulazidwa
19 Mulungu amene ali pa mpando wake kwamuyaya,
20 Mnzanga woyenda naye wathira nkhondo abwenzi ake;
21 Mawu ake ndi osalala kuposa batala
22 Tulani nkhawa zanu kwa Yehova
23 Koma Inu Mulungu mudzawatsitsa anthu oyipa