Salmos 55

NYA

1 Mvetserani pemphero langa, Inu Mulungu,

2 mverani ndipo mundiyankhe.

3 chifukwa cha mawu a adani anga,

4 Mtima wanga ukupweteka mʼkati mwanga;

5 Mantha ndi kunjenjemera zandizinga;

6 Ndinati, “Ndithu, ndikanakhala ndi mapiko ankhunda!

7 Ndikanathawira kutali

8 Ndikanathamangira kumalo anga a chitetezo;

9 Sokonezani maganizo a oyipa, Inu Ambuye, tsutsani mawu awo;

10 Usana ndi usiku iwo akuzungulirazungulira pa makoma ake;

11 Mphamvu zowononga zili pa ntchito mu mzinda;

12 Akanakhala mdani akundinyoza, ine

13 Koma iweyo mnzanga, mnzanga woyenda naye,

14 Mnzanga amene nthawi ina tinkasangalala

15 Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi;

16 Koma ine ndinafuwulira kwa Mulungu,

17 Madzulo, mmawa ndi masana

18 Iye amandiwombola ine osavulazidwa

19 Mulungu amene ali pa mpando wake kwamuyaya,

20 Mnzanga woyenda naye wathira nkhondo abwenzi ake;

21 Mawu ake ndi osalala kuposa batala

22 Tulani nkhawa zanu kwa Yehova

23 Koma Inu Mulungu mudzawatsitsa anthu oyipa

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado