Salmos 51

NYA

1 Mundichitire chifundo, Inu Mulungu,

2 Munditsuke zolakwa zanga zonse

3 Pakuti ndikudziwa mphulupulu zanga,

4 Motsutsana ndi Inu, Inu nokha, ndachimwa

5 Zoonadi ine ndinali wochimwa pomwe ndimabadwa,

6 Zoonadi inu mumafuna choonadi mu ziwalo zamʼkati mwanga;

7 Mundiyeretse ndi hisope ndipo ndidzayera,

8 Mundilole ndimve chimwemwe ndi chisangalalo,

9 Mufulatire machimo anga

10 Mulenge mʼkati mwanga mtima woyera Inu Mulungu

11 Musandichotse pamaso panu

12 Bwezeretsani mwa ine chimwemwe cha chipulumutso chanu

13 Pamenepo ndidzaphunzitsa anthu amphulupulu njira zanu

14 Mundipulumutse ku tchimo lokhetsa magazi, Inu Mulungu,

15 Inu Ambuye tsekulani milomo yanga,

16 Inu simusangalatsidwa ndi nsembe wamba.

17 Nsembe za Mulungu ndi mzimu wosweka;

18 Mwa kukoma mtima kwanu mupange Ziyoni kuti alemere;

19 Kotero kudzakhala nsembe zachilungamo,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado