1 Mundichitire chifundo, Inu Mulungu,
2 Munditsuke zolakwa zanga zonse
3 Pakuti ndikudziwa mphulupulu zanga,
4 Motsutsana ndi Inu, Inu nokha, ndachimwa
5 Zoonadi ine ndinali wochimwa pomwe ndimabadwa,
6 Zoonadi inu mumafuna choonadi mu ziwalo zamʼkati mwanga;
7 Mundiyeretse ndi hisope ndipo ndidzayera,
8 Mundilole ndimve chimwemwe ndi chisangalalo,
9 Mufulatire machimo anga
10 Mulenge mʼkati mwanga mtima woyera Inu Mulungu
11 Musandichotse pamaso panu
12 Bwezeretsani mwa ine chimwemwe cha chipulumutso chanu
13 Pamenepo ndidzaphunzitsa anthu amphulupulu njira zanu
14 Mundipulumutse ku tchimo lokhetsa magazi, Inu Mulungu,
15 Inu Ambuye tsekulani milomo yanga,
16 Inu simusangalatsidwa ndi nsembe wamba.
17 Nsembe za Mulungu ndi mzimu wosweka;
18 Mwa kukoma mtima kwanu mupange Ziyoni kuti alemere;
19 Kotero kudzakhala nsembe zachilungamo,