1 Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira ndi zoyipa, iwe munthu wamphamvu?
2 Tsiku lonse umakhalira kuganizira za kuwononga ena;
3 Iwe umakonda choyipa mʼmalo mwa kuyankhula choonadi.
4 Umakonda mawu onse opweteka,
5 Zoonadi Mulungu adzakutsitsa kupita ku chiwonongeko chamuyaya:
6 Olungama adzaona zimenezi ndi kuchita mantha;
7 “Pano tsopano pali munthu
8 Koma ine ndili ngati mtengo wa olivi
9 Ine ndidzakutamandani kwamuyaya chifukwa cha zimene mwachita;