Salmos 49

NYA

1 Imvani izi anthu a mitundu yonse;

2 anthu wamba pamodzi ndi anthu odziwika,

3 Pakamwa panga padzayankhula mawu anzeru;

4 Ndidzatchera khutu langa ku mwambo,

5 Ine ndichitirenji mantha pamene masiku oyipa afika,

6 Iwo amene adalira kulemera kwawo

7 Palibe munthu amene angawombole moyo wa mnzake

8 Dipo la moyo ndi la mtengowapatali,

9 kuti iye akhale ndi moyo mpaka muyaya

10 Pakuti onse amaona kuti anthu anzeru amamwalira;

11 Manda awo adzakhala nyumba zawo mpaka muyaya,

12 Ngakhale munthu akhale wachuma chotani,

13 Izi ndi zimene zimachitikira iwo amene amadzidalira okha,

14 Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda,

15 Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda;

16 Usavutike mu mtima pamene munthu akulemera,

17 Pakuti sadzatenga kanthu pamodzi naye pamene wamwalira,

18 Ngakhale pamene munthuyo ali moyo amadziyesa wodala,

19 iyeyo adzakakhala pamodzi ndi mʼbado wa makolo ake,

20 Munthu amene ali ndi chuma koma wopanda nzeru

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado