Salmos 48

NYA

1 Wamkulu ndi Yehova, ndi woyenera kwambiri matamando

2 Lokongola mu utali mwake,

3 Mulungu ali mu malinga ake;

4 Pamene mafumu anasonkhana pamodzi,

5 iwo anaona mzindawo ndipo anadabwa kwambiri;

6 Pomwepo anagwidwa nako kunjenjemera,

7 Inu munawawononga monga sitima zapamadzi za ku Tarisisi

8 Monga momwe tinamvera,

9 Mʼkati mwa Nyumba yanu Mulungu,

10 Monga dzina lanu, Inu Mulungu,

11 Phiri la Ziyoni likukondwera,

12 Yendayendani mu Ziyoni, uzungulireni mzindawo,

13 Yangʼanitsitsani bwino mipanda yake,

14 Pakuti Mulungu uyu ndi Mulungu wathu ku nthawi zosatha;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado