Salmos 47

NYA

1 Ombani mʼmanja, inu anthu onse;

2 Ndi woopsadi Yehova Wammwambamwamba;

3 Iye anatigonjetsera mitundu yambirimbiri ya anthu;

4 Iye anatisankhira cholowa chathu,

5 Mulungu wakwera, anthu akumufuwulira mwachimwemwe,

6 Imbani matamando kwa Mulungu, imbani matamando;

7 Pakuti Mulungu ndi mfumu ya dziko lonse lapansi;

8 Mulungu akulamulira mitundu ya anthu;

9 Anthu otchuka mwa anthu a mitundu ina asonkhana

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado