1 Ombani mʼmanja, inu anthu onse;
2 Ndi woopsadi Yehova Wammwambamwamba;
3 Iye anatigonjetsera mitundu yambirimbiri ya anthu;
4 Iye anatisankhira cholowa chathu,
5 Mulungu wakwera, anthu akumufuwulira mwachimwemwe,
6 Imbani matamando kwa Mulungu, imbani matamando;
7 Pakuti Mulungu ndi mfumu ya dziko lonse lapansi;
8 Mulungu akulamulira mitundu ya anthu;
9 Anthu otchuka mwa anthu a mitundu ina asonkhana