Salmos 46

NYA

1 Mulungu ndiye kothawira kwathu ndi mphamvu yathu,

2 Nʼchifukwa chake sitidzaopa ngakhale dziko lapansi lisunthike,

3 ngakhale madzi ake atakokoma ndi kuchita thovu,

4 Kuli mtsinje umene njira zake za madzi zimasangalatsa mzinda wa Mulungu,

5 Mulungu ali mʼkati mwake, iwo sudzagwa;

6 Mitundu ikupokosera, mafumu akugwa;

7 Yehova Wamphamvuzonse ali ndi ife,

8 Bwerani kuti mudzaone ntchito za Yehova,

9 Iye amathetsa nkhondo ku malekezero a dziko lapansi;

10 Iye akuti, “Khala chete, ndipo dziwa kuti ndine Mulungu;

11 Yehova Wamphamvuzonse ali ndi ife,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado