Salmos 45

NYA

1 Mtima wanga watakasika ndi nkhani yokoma

2 Inu ndinu abwino kwambiri kuposa anthu onse

3 Mangirirani lupanga lanu mʼchiwuno mwanu, inu munthu wamphamvu;

4 Mu ukulu wanu mupite mutakwera mwachigonjetso

5 Mivi yanu yakuthwa ilase mitima ya adani a mfumu,

6 Mpando wanu waufumu, Inu Mulungu, udzakhala ku nthawi za nthawi;

7 Inu mumakonda chilungamo ndi kudana ndi zoyipa;

8 Mikanjo yanu yonse ndi yonunkhira ndi mure ndi aloe ndi kasiya;

9 Ana aakazi a mafumu ali pakati pa akazi anu olemekezeka;

10 Tamvera, iwe mwana wa mkazi ganizira ndipo tchera khutu;

11 Mfumu yathedwa nzeru chifukwa cha kukongola kwako;

12 Mwana wa mkazi wa ku Turo adzabwera ndi mphatso,

13 Wokongola kwambiri ndi mwana wa mfumu ali mʼchipinda mwake,

14 Atavala zovala zamaluwamaluwa akupita naye kwa mfumu;

15 Iwo akuwaperekeza ndi chimwemwe ndi chisangalalo;

16 Ana ako aamuna adzatenga malo a makolo ako;

17 Ndidzabukitsa mbiri yako mʼmibado yonse;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado