Salmos 44

NYA

1 Ife tamva ndi makutu athu, Inu Mulungu;

2 Ndi dzanja lanu munathamangitsa mitundu ya anthu ena

3 Sanalande dziko ndi lupanga lawo,

4 Inu ndinu Mfumu yanga ndi Mulungu wanga

5 Kudzera kwa inu ife timabweza adani athu;

6 Sindidalira uta wanga,

7 koma Inu mumatigonjetsera adani athu,

8 Timanyadira mwa Mulungu wathu tsiku lonse,

9 Koma tsopano mwatikana ndi kutichepetsa;

10 Munachititsa ife kubwerera mʼmbuyo pamaso pa mdani

11 Inu munatipereka kuti tiwonongedwe monga nkhosa

12 Inu munagulitsa anthu anu pa mtengo wotsika,

13 Mwachititsa kuti tikhale chochititsa manyazi kwa anthu a mitundu ina,

14 Mwachititsa kuti tikhale onyozeka pakati pa anthu a mitundu ina;

15 Manyazi anga ali pamaso panga tsiku lonse

16 chifukwa cha mawu otonza a iwo amene amandinyoza ndi kundichita chipongwe,

17 Zonsezi zinatichitikira

18 Mitima yathu sinabwerere mʼmbuyo;

19 Koma Inu mwatiphwanya ndi kuchititsa kuti tikhale ozunzidwa ndi ankhandwe

20 Tikanayiwala dzina la Mulungu wathu

21 kodi Mulungu wathu sakanazidziwa zimenezi,

22 Komabe chifukwa cha Inu timakumana ndi imfa tsiku lonse,

23 Dzukani Ambuye! Nʼchifukwa chiyani mukugona!

24 Nʼchifukwa chiyani mukubisa nkhope yanu,

25 Tatsitsidwa pansi mpaka pa fumbi;

26 Imirirani ndi kutithandiza,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado