1 Onetsani kusalakwa kwanga Inu Mulungu;
2 Pajatu Inu Mulungu ndinu mphamvu zanga.
3 Tumizani kuwunika kwanu ndi choonadi chanu
4 Ndipo ndidzapita ku guwa lansembe la Mulungu,
5 Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni iwe moyo wanga?
NYA
1 Onetsani kusalakwa kwanga Inu Mulungu;
2 Pajatu Inu Mulungu ndinu mphamvu zanga.
3 Tumizani kuwunika kwanu ndi choonadi chanu
4 Ndipo ndidzapita ku guwa lansembe la Mulungu,
5 Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni iwe moyo wanga?