Salmos 42

NYA

1 Monga mbawala ipuma wefuwefu kufunafuna mitsinje yamadzi,

2 Moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Mulungu, lofuna Mulungu wamoyo.

3 Misozi yanga yakhala chakudya changa

4 Zinthu izi ndimazikumbukira

5 Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni, iwe moyo wanga?

6 Mulungu wanga.

7 Madzi akuya akuyitana madzi akuya

8 Koma usana Yehova amalamulira chikondi chake,

9 Ine ndikuti kwa Mulungu Thanthwe langa,

10 Mafupa anga ali ndi ululu wakufa nawo

11 Bwanji ukumva chisoni,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado