1 Monga mbawala ipuma wefuwefu kufunafuna mitsinje yamadzi,
2 Moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Mulungu, lofuna Mulungu wamoyo.
3 Misozi yanga yakhala chakudya changa
4 Zinthu izi ndimazikumbukira
5 Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni, iwe moyo wanga?
6 Mulungu wanga.
7 Madzi akuya akuyitana madzi akuya
8 Koma usana Yehova amalamulira chikondi chake,
9 Ine ndikuti kwa Mulungu Thanthwe langa,
10 Mafupa anga ali ndi ululu wakufa nawo
11 Bwanji ukumva chisoni,