1 Wodala ndi munthu amene amaganizira anthu osauka;
2 Yehova adzamuteteza ndi kusunga moyo wake;
3 Yehova adzamuthandiza pamene akudwala
4 Ndinati, “Inu Yehova, mundichitire chifundo;
5 Adani anga mwankhwidzi amanena za ine kuti,
6 Pamene wina abwera kudzandiona,
7 Adani anga onse amanongʼonezana pamodzi kulimbana nane,
8 “Matenda owopsa amugwira;
9 Ngakhale bwenzi langa la pamtima amene ndinamudalira,
10 Koma Yehova mundichititre chifundo,
11 Ine ndikudziwa kuti mukukondwera nane,
12 Mu ungwiro wanga Inu mumandisunga
13 Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli