1 Mofatsa ndinadikira Yehova
2 Ananditulutsa mʼdzenje lachitayiko,
3 Iye anayika nyimbo yatsopano mʼkamwa mwanga,
4 Ndi wodala munthu
5 Zambiri, Yehova Mulungu wanga,
6 Nsembe ndi zopereka Inu simuzifuna,
7 Kotero ndinati, “Ndili pano, ndabwera.
8 Ndikufuna kuchita chifuniro chanu, Inu Mulungu wanga;
9 Ndikulalikira uthenga wa chilungamo chanu mu msonkhano waukulu;
10 Sindibisa chilungamo chanu mu mtima mwanga;
11 Musandichotsere chifundo chanu Yehova;
12 Pakuti mavuto osawerengeka andizungulira;
13 Pulumutseni Yehova;
14 Onse amene akufunafuna kuchotsa moyo wanga
15 Iwo amene amanena kwa ine kuti, “Hee! Hee!”
16 Koma iwo amene amafunafuna Inu
17 Komabe Ine ndine wosauka ndi wosowa;