Salmos 40

NYA

1 Mofatsa ndinadikira Yehova

2 Ananditulutsa mʼdzenje lachitayiko,

3 Iye anayika nyimbo yatsopano mʼkamwa mwanga,

4 Ndi wodala munthu

5 Zambiri, Yehova Mulungu wanga,

6 Nsembe ndi zopereka Inu simuzifuna,

7 Kotero ndinati, “Ndili pano, ndabwera.

8 Ndikufuna kuchita chifuniro chanu, Inu Mulungu wanga;

9 Ndikulalikira uthenga wa chilungamo chanu mu msonkhano waukulu;

10 Sindibisa chilungamo chanu mu mtima mwanga;

11 Musandichotsere chifundo chanu Yehova;

12 Pakuti mavuto osawerengeka andizungulira;

13 Pulumutseni Yehova;

14 Onse amene akufunafuna kuchotsa moyo wanga

15 Iwo amene amanena kwa ine kuti, “Hee! Hee!”

16 Koma iwo amene amafunafuna Inu

17 Komabe Ine ndine wosauka ndi wosowa;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado