1 Ndinati, “Ndidzasamalira njira zanga
2 Koma pamene ndinali chete
3 Mtima wanga unatentha mʼkati mwanga,
4 “Yehova ndionetseni mathero a moyo wanga
5 Inu mwachititsa kuti masiku anga akhale ochepa kwambiri,
6 Munthu ali ngati chithunzithunzi chake pamene akuyenda uku ndi uku:
7 “Koma tsopano Ambuye kodi ndifunanso chiyani?
8 Pulumutseni ku zolakwa zanga zonse;
9 Ine ndinali chete; sindinatsekule pakamwa panga
10 Chotsani mkwapulo wanu pa ine;
11 Inu mumadzudzula ndi kulanga anthu chifukwa cha tchimo lawo;
12 “Imvani pemphero langa Inu Yehova,
13 Musandiyangʼane mwaukali, choncho ndidzatha kusangalala