Salmos 39

NYA

1 Ndinati, “Ndidzasamalira njira zanga

2 Koma pamene ndinali chete

3 Mtima wanga unatentha mʼkati mwanga,

4 “Yehova ndionetseni mathero a moyo wanga

5 Inu mwachititsa kuti masiku anga akhale ochepa kwambiri,

6 Munthu ali ngati chithunzithunzi chake pamene akuyenda uku ndi uku:

7 “Koma tsopano Ambuye kodi ndifunanso chiyani?

8 Pulumutseni ku zolakwa zanga zonse;

9 Ine ndinali chete; sindinatsekule pakamwa panga

10 Chotsani mkwapulo wanu pa ine;

11 Inu mumadzudzula ndi kulanga anthu chifukwa cha tchimo lawo;

12 “Imvani pemphero langa Inu Yehova,

13 Musandiyangʼane mwaukali, choncho ndidzatha kusangalala

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado