1 Yehova musandidzudzule mutapsa mtima
2 Pakuti mivi yanu yandilasa,
3 Chifukwa cha ukali wanu mulibe thanzi mʼthupi langa;
4 Kulakwa kwanga kwandipsinja
5 Mabala anga akuwola ndipo akununkha
6 Ine ndapindika msana ndipo ndawerama kwambiri;
7 Msana wanga wagwidwa ndi ululu wosasimbika,
8 Ndilibe mphamvu ndipo ndakunthidwa kwathunthu;
9 Zokhumba zanga zonse zili poonekera pamaso panu Ambuye,
10 Mtima wanga ukugunda, mphamvu zanga zikutha;
11 Abwenzi anga ndi anzanga akundipewa chifukwa cha mabala anga;
12 Iwo amene akufunafuna moyo wanga atchera misampha yawo,
13 Ine ndili ngati munthu wosamva amene sangamve,
14 Ndakhala ngati munthu amene samva,
15 Ndikudikira Inu Yehova;
16 Pakuti Ine ndinati, “Musawalole kuti akondwere
17 Pakuti ndili pafupi kugwa,
18 Ndikuvomereza mphulupulu zanga;
19 Ambiri ndi adani anga amphamvu;
20 Iwo amene amandibwezera zoyipa mʼmalo mwa zabwino
21 Inu Yehova, musanditaye;
22 Bwerani msanga kudzandithandiza,