Salmos 38

NYA

1 Yehova musandidzudzule mutapsa mtima

2 Pakuti mivi yanu yandilasa,

3 Chifukwa cha ukali wanu mulibe thanzi mʼthupi langa;

4 Kulakwa kwanga kwandipsinja

5 Mabala anga akuwola ndipo akununkha

6 Ine ndapindika msana ndipo ndawerama kwambiri;

7 Msana wanga wagwidwa ndi ululu wosasimbika,

8 Ndilibe mphamvu ndipo ndakunthidwa kwathunthu;

9 Zokhumba zanga zonse zili poonekera pamaso panu Ambuye,

10 Mtima wanga ukugunda, mphamvu zanga zikutha;

11 Abwenzi anga ndi anzanga akundipewa chifukwa cha mabala anga;

12 Iwo amene akufunafuna moyo wanga atchera misampha yawo,

13 Ine ndili ngati munthu wosamva amene sangamve,

14 Ndakhala ngati munthu amene samva,

15 Ndikudikira Inu Yehova;

16 Pakuti Ine ndinati, “Musawalole kuti akondwere

17 Pakuti ndili pafupi kugwa,

18 Ndikuvomereza mphulupulu zanga;

19 Ambiri ndi adani anga amphamvu;

20 Iwo amene amandibwezera zoyipa mʼmalo mwa zabwino

21 Inu Yehova, musanditaye;

22 Bwerani msanga kudzandithandiza,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado