1 Uthenga uli mu mtima mwanga
2 Pakuti iye mʼkuona kwake amadzinyenga yekha kwambiri,
3 Mawu a pakamwa pake ndi oyipa ndi achinyengo;
4 Ngakhale ali pa bedi pake amakonzekera zoyipa;
5 Chikondi chanu Yehova, chimafika ku mayiko a kumwamba,
6 Chilungamo chanu Mulungu chili ngati mapiri aakulu,
7 Chikondi chanu chosatha ndi chamtengowapatali!
8 Iwo amadyerera zinthu zambiri za mʼnyumba yanu;
9 Pakuti kwa Inu kuli kasupe wamoyo;
10 Pitirizani chikondi chanu pa iwo amene amakudziwani,
11 Musalole kuti phazi la wodzikuza libwere kulimbana nane,
12 Onani momwe ochita zoyipa agonera atagwa,