Salmos 36

NYA

1 Uthenga uli mu mtima mwanga

2 Pakuti iye mʼkuona kwake amadzinyenga yekha kwambiri,

3 Mawu a pakamwa pake ndi oyipa ndi achinyengo;

4 Ngakhale ali pa bedi pake amakonzekera zoyipa;

5 Chikondi chanu Yehova, chimafika ku mayiko a kumwamba,

6 Chilungamo chanu Mulungu chili ngati mapiri aakulu,

7 Chikondi chanu chosatha ndi chamtengowapatali!

8 Iwo amadyerera zinthu zambiri za mʼnyumba yanu;

9 Pakuti kwa Inu kuli kasupe wamoyo;

10 Pitirizani chikondi chanu pa iwo amene amakudziwani,

11 Musalole kuti phazi la wodzikuza libwere kulimbana nane,

12 Onani momwe ochita zoyipa agonera atagwa,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado