1 Ndidzayamika Yehova nthawi zonse;
2 Moyo wanga udzanyadira Yehova;
3 Lemekezani Yehova pamodzi ndi ine;
4 Ine ndinafunafuna Yehova ndipo Iye anandiyankha;
5 Iwo amene amayangʼana kwa Iye, nkhope zawo zimanyezimira;
6 Munthu wosauka uno anayitana, ndipo Yehova anamumva;
7 Mngelo wa Yehova amatchinjiriza amene amakonda Iye
8 Lawani ndipo onani kuti Yehova ndi wabwino;
9 Wopani Yehova inu oyera mtima ake,
10 Mikango itha kulefuka ndi kumva njala
11 Bwerani ana anga, mundimvere;
12 Aliyense wa inu amene amakonda moyo wake
13 asunge lilime lake ku zoyipa
14 Tembenuka kuchoka ku zoyipa ndipo chita zabwino;
15 Maso a Yehova ali pa olungama
16 nkhope ya Yehova ikutsutsana ndi amene amachita zoyipa,
17 Olungama amafuwula, ndipo Yehova amawamva;
18 Yehova ali pafupi kwa osweka mtima
19 Munthu wolungama atha kukhala ndi mavuto ambiri,
20 Iye amateteza mafupa ake onse,
21 Choyipa chidzapha anthu oyipa;
22 Yehova amawombola atumiki ake;