Salmos 34

NYA

1 Ndidzayamika Yehova nthawi zonse;

2 Moyo wanga udzanyadira Yehova;

3 Lemekezani Yehova pamodzi ndi ine;

4 Ine ndinafunafuna Yehova ndipo Iye anandiyankha;

5 Iwo amene amayangʼana kwa Iye, nkhope zawo zimanyezimira;

6 Munthu wosauka uno anayitana, ndipo Yehova anamumva;

7 Mngelo wa Yehova amatchinjiriza amene amakonda Iye

8 Lawani ndipo onani kuti Yehova ndi wabwino;

9 Wopani Yehova inu oyera mtima ake,

10 Mikango itha kulefuka ndi kumva njala

11 Bwerani ana anga, mundimvere;

12 Aliyense wa inu amene amakonda moyo wake

13 asunge lilime lake ku zoyipa

14 Tembenuka kuchoka ku zoyipa ndipo chita zabwino;

15 Maso a Yehova ali pa olungama

16 nkhope ya Yehova ikutsutsana ndi amene amachita zoyipa,

17 Olungama amafuwula, ndipo Yehova amawamva;

18 Yehova ali pafupi kwa osweka mtima

19 Munthu wolungama atha kukhala ndi mavuto ambiri,

20 Iye amateteza mafupa ake onse,

21 Choyipa chidzapha anthu oyipa;

22 Yehova amawombola atumiki ake;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado