Salmos 33

NYA

1 Imbirani Yehova mokondwera Inu olungama,

2 Mutamandeni Yehova ndi pangwe;

3 Muyimbireni nyimbo yatsopano;

4 Pakuti mawu a Yehova ndi olungama ndi owona;

5 Yehova amakonda chilungamo ndipo amaweruza molungama;

6 Ndi mawu a Yehova mayiko akumwamba anapangidwa,

7 Iye amasonkhanitsa pamodzi madzi a mʼnyanja mʼmitsuko;

8 Dziko lonse lapansi liope Yehova;

9 Pakuti Iye anayankhula ndipo zinakhalapo;

10 Yehova amalepheretsa chikonzero cha anthu a mitundu ina;

11 Koma chikonzero cha Yehova chimakhala mpaka muyaya,

12 Wodala mtundu wa anthu umene Mulungu wake ndi Yehova,

13 Kuchokera kumwamba Yehova amayangʼana pansi

14 kuchokera ku malo ake okhalako Iye amayangʼanira

15 Iye amene amapanga mitima ya onse,

16 Palibe mfumu imene imapulumutsidwa chifukwa cha kukula kwa gulu lake lankhondo;

17 Kavalo ndi chiyembekezo cha chabechabe cha chipulumutso,

18 Koma maso a Yehova ali pa iwo amene amaopa Iye;

19 kuwawombola iwo ku imfa

20 Ife timadikira kwa Yehova mwachiyembekezo;

21 Mwa Iye mitima yathu imakondwera,

22 Chikondi chanu chosatha

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado