1 Ngodala munthu
2 Ngodala munthu
3 Pamene ndinali chete,
4 Pakuti usana ndi usiku
5 Kotero ine ndinavomereza tchimo langa kwa Inu,
6 Choncho aliyense okhulupirika apemphere kwa Inuyo
7 Inu ndi malo anga obisala;
8 Ndidzakulangiza ndi kukuphunzitsa njira imene udzayendamo;
9 Usakhale ngati kavalo kapena bulu,
10 Zowawa ndi zambiri za anthu oyipa
11 Kondwerani mwa Yehova inu olungama;