Salmos 31

NYA

1 Mwa Inu Yehova, ine ndimathawiramo;

2 Tcherani khutu lanu kwa ine,

3 Popeza Inu ndinu thanthwe langa ndi linga langa,

4 Ndimasuleni mu msampha umene anditchera

5 Mʼmanja mwanu ndipereka mzimu wanga;

6 Koma ine ndimadana nawo amene amamamatira mafano achabechabe;

7 Ndidzakondwa ndi kusangalala mʼchikondi chanu

8 Inu simunandipereke kwa mdani

9 Mundichitire chifundo Inu Yehova pakuti ndili pa mavuto;

10 Moyo wanga ukunyeka chifukwa cha kuwawidwa mtima

11 Chifukwa cha adani anga onse,

12 Ine ndinayiwalika kwa iwo ngati kuti ndinamwalira;

13 Pakuti ine ndamva zonena zoyipa za anthu ambiri;

14 Koma ndikudalira Inu Yehova;

15 Masiku anga ali mʼmanja mwanu;

16 Walitsani nkhope yanu pa mtumiki wanu;

17 Yehova musalole kuti ndichite manyazi,

18 Milomo yawo yabodzayo ikhale chete,

19 Ndi waukulu ubwino wanu

20 Mu mthunzi wa pamalo popezeka panu muwabisa,

21 Matamando akhale kwa Yehova,

22 Ndili mʼnkhawa zanga ndinati,

23 Kondani Yehova oyera mtima ake onse!

24 Khalani ndi nyonga ndipo limbani mtima,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado