1 Ndidzakukwezani Yehova,
2 Inu Yehova Mulungu wanga ndinapempha kwa Inu thandizo
3 Inu Yehova, munanditulutsa ku manda,
4 Imbirani Yehova inu anthu ake okhulupirika;
5 Pakuti mkwiyo wake umakhala kwa kanthawi
6 Pamene ndinaona kuti ndili otetezedwa ndinati,
7 Inu Yehova, pamene munandikomera mtima,
8 Kwa Inu Yehova ndinayitana;
9 “Kodi pali phindu lanji powonongeka kwanga
10 Imvani Yehova ndipo mundichitire chifundo;
11 Inu munasandutsa kulira kwanga kukhala kuvina;
12 kuti mtima wanga uthe kuyimbira Inu usakhale chete.