Salmos 30

NYA

1 Ndidzakukwezani Yehova,

2 Inu Yehova Mulungu wanga ndinapempha kwa Inu thandizo

3 Inu Yehova, munanditulutsa ku manda,

4 Imbirani Yehova inu anthu ake okhulupirika;

5 Pakuti mkwiyo wake umakhala kwa kanthawi

6 Pamene ndinaona kuti ndili otetezedwa ndinati,

7 Inu Yehova, pamene munandikomera mtima,

8 Kwa Inu Yehova ndinayitana;

9 “Kodi pali phindu lanji powonongeka kwanga

10 Imvani Yehova ndipo mundichitire chifundo;

11 Inu munasandutsa kulira kwanga kukhala kuvina;

12 kuti mtima wanga uthe kuyimbira Inu usakhale chete.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado