1 Perekani kwa Yehova, inu anthu amphamvu,
2 Perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake,
3 Liwu la Yehova lili pamwamba pa madzi;
4 Liwu la Yehova ndi lamphamvu;
5 Liwu la Yehova limathyola mikungudza;
6 Iye amachititsa Lebanoni kulumphalumpha ngati mwana wangʼombe,
7 Liwu la Yehova limakantha
8 Liwu la Yehova limagwedeza chipululu;
9 Liwu la Yehova limapindapinda mibawa
10 Yehova amakhala pamwamba pa madzi osefukira,
11 Yehova amapereka mphamvu kwa anthu ake;