Salmos 29

NYA

1 Perekani kwa Yehova, inu anthu amphamvu,

2 Perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake,

3 Liwu la Yehova lili pamwamba pa madzi;

4 Liwu la Yehova ndi lamphamvu;

5 Liwu la Yehova limathyola mikungudza;

6 Iye amachititsa Lebanoni kulumphalumpha ngati mwana wangʼombe,

7 Liwu la Yehova limakantha

8 Liwu la Yehova limagwedeza chipululu;

9 Liwu la Yehova limapindapinda mibawa

10 Yehova amakhala pamwamba pa madzi osefukira,

11 Yehova amapereka mphamvu kwa anthu ake;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado