1 Kwa Inu ine ndiyitana, Yehova ndinu Thanthwe langa;
2 Imvani kupempha chifundo kwanga
3 Musandikokere kutali pamodzi ndi anthu oyipa,
4 Muwabwezere chifukwa cha zochita zawo
5 Popeza iwowo sakhudzidwa ndi ntchito za Yehova,
6 Matamando apite kwa Yehova,
7 Yehova ndiye mphamvu yanga ndi chishango changa;
8 Yehova ndi mphamvu ya anthu ake,
9 Pulumutsani anthu anu ndipo mudalitse cholowa chanu;