Salmos 28

NYA

1 Kwa Inu ine ndiyitana, Yehova ndinu Thanthwe langa;

2 Imvani kupempha chifundo kwanga

3 Musandikokere kutali pamodzi ndi anthu oyipa,

4 Muwabwezere chifukwa cha zochita zawo

5 Popeza iwowo sakhudzidwa ndi ntchito za Yehova,

6 Matamando apite kwa Yehova,

7 Yehova ndiye mphamvu yanga ndi chishango changa;

8 Yehova ndi mphamvu ya anthu ake,

9 Pulumutsani anthu anu ndipo mudalitse cholowa chanu;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado