1 Yehova ndiye kuwunika kwanga ndi chipulumutso changa;
2 Pamene anthu oyipa abwera kudzalimbana nane
3 Ngakhale gulu lankhondo lindizinge,
4 Chinthu chimodzi chokha chimene ndipempha kwa Yehova,
5 Pakuti pa tsiku la msautso
6 Kotero mutu wanga udzakwezedwa
7 Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu Yehova
8 Mtima wanga ukuti kwa Inu, “Funafuna nkhope yake!”
9 Musandibisire nkhope yanu,
10 Ngakhale abambo ndi amayi anga anditaya
11 Phunzitseni njira yanu Inu Yehova,
12 Musandipereke ku zokhumba za adani anga,
13 Ine ndikutsimikiza mtima za zimenezi;
14 Dikirani pa Yehova;