Salmos 27

NYA

1 Yehova ndiye kuwunika kwanga ndi chipulumutso changa;

2 Pamene anthu oyipa abwera kudzalimbana nane

3 Ngakhale gulu lankhondo lindizinge,

4 Chinthu chimodzi chokha chimene ndipempha kwa Yehova,

5 Pakuti pa tsiku la msautso

6 Kotero mutu wanga udzakwezedwa

7 Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu Yehova

8 Mtima wanga ukuti kwa Inu, “Funafuna nkhope yake!”

9 Musandibisire nkhope yanu,

10 Ngakhale abambo ndi amayi anga anditaya

11 Phunzitseni njira yanu Inu Yehova,

12 Musandipereke ku zokhumba za adani anga,

13 Ine ndikutsimikiza mtima za zimenezi;

14 Dikirani pa Yehova;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado