Salmos 26

NYA

1 Weruzeni Inu Yehova

2 Patseni mayeso, Inu Yehova ndipo ndiyeseni,

3 pakuti chikondi chanu chili pamaso panga nthawi zonse,

4 Ine sindikhala pansi pamodzi ndi anthu achinyengo,

5 Ndimanyansidwa ndi msonkhano wa anthu ochita zoyipa

6 Ndimasamba mʼmanja mwanga kuonetsa kusalakwa kwanga

7 kulengeza mofuwula za matamando anu

8 Ndimakonda Nyumba imene Inu Yehova mumakhalamo,

9 Musachotse moyo wanga pamodzi ndi ochimwa,

10 amene mʼmanja mwawo muli ndondomeko zoyipa,

11 Koma ine ndimakhala moyo wosalakwa;

12 Ndayima pa malo wopanda zovuta

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado