1 Kwa Inu Yehova, ndipereka moyo wanga.
2 Ndimadalira Inu Mulungu wanga.
3 Aliyense amene amayembekezera kwa Ambuye
4 Ndidziwitseni njira zanu Inu Yehova,
5 tsogolereni mʼchoonadi chanu ndi kundiphunzitsa,
6 Kumbukirani Inu Yehova chifundo ndi chikondi chanu chachikulu,
7 Musakumbukire machimo a ubwana wanga
8 Yehova ndi wabwino ndi wolungama;
9 Amatsogolera odzichepetsa kuti achite zolungama
10 Njira zonse za Yehova ndi zachikondi ndi zokhulupirika
11 Chifukwa cha dzina lanu, Inu Yehova,
12 Tsono ndani munthu amene amaopa Yehova?
13 Iye adzakhala pa ulemerero masiku ake onse,
14 Yehova amawulula chinsinsi chake kwa iwo amene amamuopa;
15 Maso anga ali pa Yehova nthawi zonse,
16 Tembenukirani kwa ine ndipo mundikomere mtima,
17 Masautso a mu mtima mwanga achulukirachulukira;
18 Penyani mazunzo anga ndi zovuta zanga
19 Onani mmene adani anga achulukira
20 Tetezani moyo wanga ndi kundilanditsa;
21 Kukhulupirika ndi kulungama kwanga kunditeteze,
22 Wombolani Israeli Inu Mulungu,