1 Dziko lapansi ndi la Yehova ndi zonse zimene zili mʼmenemo,
2 pakuti Iye ndiye anayika maziko ake pa nyanja
3 Ndani angakwere phiri la Yehova?
4 Iye amene ali ndi mʼmanja moyera ndi mtima woyera,
5 Iyeyo adzalandira madalitso kwa Yehova
6 Umenewo ndiwo mʼbado wa amene amafunafuna Yehova;
7 Tukulani mitu yanu inu zipata;
8 Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani?
9 Tukulani mitu yanu, inu zipata;
10 Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani?