1 Inu Yehova, mfumu ikusangalala mu mphamvu yanu,
2 Inu mwayipatsa zokhumba za mtima wake
3 Inu munayilandira ndi madalitso ochuluka
4 Iye anakupemphani moyo, ndipo munamupatsa
5 Kudzera mʼzigonjetso zimene munapereka, ulemerero wake ndi waukulu;
6 Zoonadi Inu mwayipatsa madalitso amuyaya,
7 Pakuti mfumu imadalira Yehova;
8 Dzanja lanu lidzayimitsa adani anu onse;
9 Pa nthawi ya kuonekera kwanu
10 Inu mudzawononga ana awo pa dziko lapansi,
11 Ngakhale iwo akukonzereni chiwembu mwa kuchenjera kwawo
12 pakuti mudzawapirikitsa ndipo adzaonetsa misana yawo
13 Mukwezeke Inu Yehova mʼmphamvu yanu,