1 Yehova akuyankhe pamene uli pa msautso;
2 Iye atumize thandizo kuchokera ku malo ake opatulika;
3 Iye akumbukire nsembe zako zonse
4 Akupatse chokhumba cha mtima wako
5 Ife tidzafuwula ndi chimwemwe pamene iwe wapambana
6 Tsopano ndadziwa kuti Yehova amapulumutsa wodzozedwa wake;
7 Ena amadalira magaleta ndipo ena akavalo
8 Iwo amagonjetsedwa ndi kugwa,
9 Inu Yehova, pulumutsani mfumu!