Salmos 20

NYA

1 Yehova akuyankhe pamene uli pa msautso;

2 Iye atumize thandizo kuchokera ku malo ake opatulika;

3 Iye akumbukire nsembe zako zonse

4 Akupatse chokhumba cha mtima wako

5 Ife tidzafuwula ndi chimwemwe pamene iwe wapambana

6 Tsopano ndadziwa kuti Yehova amapulumutsa wodzozedwa wake;

7 Ena amadalira magaleta ndipo ena akavalo

8 Iwo amagonjetsedwa ndi kugwa,

9 Inu Yehova, pulumutsani mfumu!

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado