1 Zakumwamba zimalengeza za ulemerero wa Mulungu;
2 Tsiku ndi tsiku zimayankhula mawu ambiri,
3 Palibe kuyankhula, palibe mawu aliwonse;
4 Koma uthenga wawo umapita pa dziko lonse lapansi,
5 Dzuwa lili ngati mkwatibwi wobwera kuchokera ku nsanja yake,
6 Limatuluka kuyambira mbali ina ya thambo
7 Lamulo la Yehova ndi langwiro,
8 Malangizo a Yehova ndi olungama,
9 Kuopa Yehova ndiye chinthu changwiro,
10 ndi a mtengowapatali kuposa golide,
11 Mtumiki wanu amachenjezedwa nawo;
12 Ndani angathe kudziwa zolakwa zake?
13 Muteteze mtumiki wanunso ku machimo ochita akudziwa;
14 Mawu a mʼkamwa mwanga ndi zolingalira za mu mtima mwanga