Salmos 19

NYA

1 Zakumwamba zimalengeza za ulemerero wa Mulungu;

2 Tsiku ndi tsiku zimayankhula mawu ambiri,

3 Palibe kuyankhula, palibe mawu aliwonse;

4 Koma uthenga wawo umapita pa dziko lonse lapansi,

5 Dzuwa lili ngati mkwatibwi wobwera kuchokera ku nsanja yake,

6 Limatuluka kuyambira mbali ina ya thambo

7 Lamulo la Yehova ndi langwiro,

8 Malangizo a Yehova ndi olungama,

9 Kuopa Yehova ndiye chinthu changwiro,

10 ndi a mtengowapatali kuposa golide,

11 Mtumiki wanu amachenjezedwa nawo;

12 Ndani angathe kudziwa zolakwa zake?

13 Muteteze mtumiki wanunso ku machimo ochita akudziwa;

14 Mawu a mʼkamwa mwanga ndi zolingalira za mu mtima mwanga

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado