Salmos 22

NYA

1 Mulungu wanga, Mulungu wanga, nʼchifukwa chiyani mwandisiya?

2 Inu Mulungu wanga, ine ndimalira masana, koma simuyankha,

3 Inu ndinu Woyera, wokhala pa mpando waufumu;

4 Pa inu makolo athu anadalira;

5 Analirira kwa inu ndipo munawapulumutsa.

6 Koma ine ndine nyongolotsi osati munthu,

7 Onse amene amandiona amandiseka;

8 “Iyeyu amadalira Yehova,

9 Komabe Inu ndinu amene munandibadwitsa, munanditulutsa mʼmimba mwa amayi anga.

10 Chibadwire ine ndinaperekedwa kwa Inu;

11 Musakhale kutali ndi ine,

12 Ngʼombe zazimuna zandizungulira;

13 Mikango yobangula pokadzula nyama,

14 Ine ndatayika pansi ngati madzi

15 Mphamvu zanga zauma ngati phale,

16 Agalu andizungulira;

17 Ine nditha kuwerenga mafupa anga onse;

18 Iwo agawana zovala zanga pakati pawo

19 Koma Inu Yehova, musakhale kutali;

20 Pulumutsani moyo wanga ku lupanga,

21 Ndilanditseni mʼkamwa mwa mikango;

22 Ine ndidzalengeza dzina lanu kwa abale anga;

23 Inu amene mumaopa Yehova mutamandeni!

24 Pakuti Iye sanapeputse kapena kunyoza

25 Ndidzakutamandani pa msonkhano waukulu chifukwa cha zimene mwandichitira.

26 Osauka adzadya ndipo adzakhuta;

27 Malekezero onse a dziko lapansi

28 pakuti ulamuliro ndi wake wa Yehova

29 Anthu olemera onse a dziko lapansi adzachita phwando ndi kulambira;

30 Zidzukulu zamʼtsogolo zidzamutumikira Iye;

31 Iwo adzalengeza za chilungamo chake

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado