1 Mulungu wanga, Mulungu wanga, nʼchifukwa chiyani mwandisiya?
2 Inu Mulungu wanga, ine ndimalira masana, koma simuyankha,
3 Inu ndinu Woyera, wokhala pa mpando waufumu;
4 Pa inu makolo athu anadalira;
5 Analirira kwa inu ndipo munawapulumutsa.
6 Koma ine ndine nyongolotsi osati munthu,
7 Onse amene amandiona amandiseka;
8 “Iyeyu amadalira Yehova,
9 Komabe Inu ndinu amene munandibadwitsa, munanditulutsa mʼmimba mwa amayi anga.
10 Chibadwire ine ndinaperekedwa kwa Inu;
11 Musakhale kutali ndi ine,
12 Ngʼombe zazimuna zandizungulira;
13 Mikango yobangula pokadzula nyama,
14 Ine ndatayika pansi ngati madzi
15 Mphamvu zanga zauma ngati phale,
16 Agalu andizungulira;
17 Ine nditha kuwerenga mafupa anga onse;
18 Iwo agawana zovala zanga pakati pawo
19 Koma Inu Yehova, musakhale kutali;
20 Pulumutsani moyo wanga ku lupanga,
21 Ndilanditseni mʼkamwa mwa mikango;
22 Ine ndidzalengeza dzina lanu kwa abale anga;
23 Inu amene mumaopa Yehova mutamandeni!
24 Pakuti Iye sanapeputse kapena kunyoza
25 Ndidzakutamandani pa msonkhano waukulu chifukwa cha zimene mwandichitira.
26 Osauka adzadya ndipo adzakhuta;
27 Malekezero onse a dziko lapansi
28 pakuti ulamuliro ndi wake wa Yehova
29 Anthu olemera onse a dziko lapansi adzachita phwando ndi kulambira;
30 Zidzukulu zamʼtsogolo zidzamutumikira Iye;
31 Iwo adzalengeza za chilungamo chake