1 Imvani Inu Yehova pempho langa lachilungamo;
2 Kusalakwa kwanga kuchokera kwa inu;
3 Ngakhale Inu mutafufuza mtima wanga ndi kundisanthula usiku,
4 Kunena za ntchito za anthu,
5 Mayendedwe anga akhazikika pa njira zanu;
6 Ine ndikuyitana Inu, Mulungu wanga, pakuti mudzandiyankha;
7 Onetsani kudabwitsa kwa chikondi chanu chachikulu,
8 Mundisunge ine ngati mwanadiso;
9 kuchoka kwa oyipa amene amandizinga ine,
10 Iwo amatseka mitima yawo yopanda chifundo,
11 Andisaka, tsopano andizungulira
12 Iwo ali ngati mkango wofuna nyama;
13 Dzukani Yehova, mulimbane nawo ndipo muwagwetse pansi;
14 Inu Yehova, pulumutseni ndi dzanja lanu kwa anthu otere,
15 Ndipo ine mʼchilungamo ndidzaona nkhope yanu;