Salmos 16

NYA

1 Ndisungeni Inu Mulungu,

2 Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga;

3 Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko,

4 Anthu amene amathamangira kwa milungu ina

5 Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa;

6 Malire a malo anga akhala pabwino;

7 Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu;

8 Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse.

9 Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera;

10 chifukwa Inu simudzandisiya ku manda,

11 Inu mwandidziwitsa njira ya moyo;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado