1 Ndisungeni Inu Mulungu,
2 Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga;
3 Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko,
4 Anthu amene amathamangira kwa milungu ina
5 Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa;
6 Malire a malo anga akhala pabwino;
7 Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu;
8 Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse.
9 Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera;
10 chifukwa Inu simudzandisiya ku manda,
11 Inu mwandidziwitsa njira ya moyo;