Salmos 15

NYA

1 Yehova, ndani angathe kukhala mʼmalo anu opatulika?

2 Munthu wa makhalidwe abwino,

3 ndipo mʼkamwa mwake simutuluka mawu osinjirira,

4 amene sapereka ulemu kwa munthu woyipa.

5 amene amakongoletsa ndalama zake popanda chiwongoladzanja

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado