Salmos 14

NYA

1 Chitsiru chimati mu mtima mwake,

2 Yehova kumwamba wayangʼana pansi,

3 Onse atembenukira kumbali,

4 Kodi anthu ochita zoyipawa sadziwa chilichonse?

5 Awo ali apowo, agwidwa ndi mantha aakulu,

6 Inu ochita zoyipa mumalepheretsa chikonzero cha anthu osauka,

7 Ndithu, chipulumutso cha Israeli chidzachokera ku Ziyoni!

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado