1 Chitsiru chimati mu mtima mwake,
2 Yehova kumwamba wayangʼana pansi,
3 Onse atembenukira kumbali,
4 Kodi anthu ochita zoyipawa sadziwa chilichonse?
5 Awo ali apowo, agwidwa ndi mantha aakulu,
6 Inu ochita zoyipa mumalepheretsa chikonzero cha anthu osauka,
7 Ndithu, chipulumutso cha Israeli chidzachokera ku Ziyoni!