1 Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?
2 Ndidzalimbana ndi maganizo anga
3 Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.
4 mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”
5 Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;
6 Ine ndidzayimbira Yehova