Salmos 13

NYA

1 Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?

2 Ndidzalimbana ndi maganizo anga

3 Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.

4 mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”

5 Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;

6 Ine ndidzayimbira Yehova

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado