1 Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika;
2 Aliyense amanamiza mʼbale wake;
3 Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo
4 Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu;
5 “Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu
6 Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro
7 Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo
8 Oyipa amangoyendayenda ponseponse