Salmos 144

NYA

1 Atamandike Yehova Thanthwe langa,

2 Iye ndiye Mulungu wanga wachikondi ndi malo anga otetezedwa,

3 Inu Yehova, munthu nʼchiyani kuti mumamusamalira,

4 Munthu ali ngati mpweya;

5 Ngʼambani mayiko akumwamba, Inu Yehova, ndipo tsikani pansi;

6 Tumizani zingʼaningʼani ndi kubalalitsa adani;

7 Tambasulani dzanja lanu kuchokera kumwamba;

8 amene pakamwa pawo ndi podzala ndi mabodza,

9 Ndidzakuyimbirani nyimbo yatsopano Inu Mulungu;

10 kwa Iye amene amapambanitsa mafumu,

11 Landitseni ndi kundipulumutsa,

12 Ndipo ana aamuna pa chinyamata chawo

13 Nkhokwe zathu zidzakhala zodzaza

14 Ngʼombe zathu zidzanyamula katundu wolemera.

15 Odala anthu amene adzalandira madalitso awa;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado