Salmos 143

NYA

1 Yehova imvani pemphero langa,

2 Musazenge mlandu mtumiki wanu,

3 Mdani akundithamangitsa,

4 Choncho mzimu wanga ukufowoka mʼkati mwanga;

5 Ndimakumbukira masiku amakedzana;

6 Ndatambalitsa manja anga kwa Inu;

7 Yehova ndiyankheni msanga;

8 Lolani kuti mmawa ubweretse mawu achikondi chanu chosasinthika,

9 Pulumutseni kwa adani anga, Inu Yehova,

10 Phunzitseni kuchita chifuniro chanu,

11 Sungani moyo wanga Inu Yehova chifukwa cha dzina lanu;

12 Mwa chikondi chanu chosasinthika khalitsani chete adani anga;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado