1 Yehova imvani pemphero langa,
2 Musazenge mlandu mtumiki wanu,
3 Mdani akundithamangitsa,
4 Choncho mzimu wanga ukufowoka mʼkati mwanga;
5 Ndimakumbukira masiku amakedzana;
6 Ndatambalitsa manja anga kwa Inu;
7 Yehova ndiyankheni msanga;
8 Lolani kuti mmawa ubweretse mawu achikondi chanu chosasinthika,
9 Pulumutseni kwa adani anga, Inu Yehova,
10 Phunzitseni kuchita chifuniro chanu,
11 Sungani moyo wanga Inu Yehova chifukwa cha dzina lanu;
12 Mwa chikondi chanu chosasinthika khalitsani chete adani anga;