1 Ndikulirira Yehova mofuwula;
2 Ndikukhuthula madandawulo anga pamaso pake;
3 Pamene mzimu wanga walefuka mʼkati mwanga,
4 Yangʼanani kumanja kwanga ndipo onani;
5 Ndilirira Inu Yehova;
6 Mverani kulira kwanga
7 Tulutseni mʼndende yanga
NYA
1 Ndikulirira Yehova mofuwula;
2 Ndikukhuthula madandawulo anga pamaso pake;
3 Pamene mzimu wanga walefuka mʼkati mwanga,
4 Yangʼanani kumanja kwanga ndipo onani;
5 Ndilirira Inu Yehova;
6 Mverani kulira kwanga
7 Tulutseni mʼndende yanga