Salmos 141

NYA

1 Inu Yehova ndikukuyitanani; bwerani msanga kwa ine.

2 Pemphero langa lifike kwa Inu ngati lubani;

3 Yehova ikani mlonda pakamwa panga;

4 Musalole kuti mtima wanga ukokedwere ku zoyipa;

5 Munthu wolungama andikanthe, chimenecho ndiye chifundo;

6 Olamulira awo adzaponyedwa pansi kuchokera pa malo okwera kwambiri,

7 Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza,

8 Koma maso anga akupenyetsetsa Inu Ambuye Wamphamvuzonse;

9 Mundipulumutse ku misampha imene anditchera,

10 Anthu oyipa akodwe mʼmaukonde awo,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado