Salmos 140

NYA

1 Landitseni Yehova kwa anthu oyipa;

2 amene mu mtima mwawo amakonza zinthu zoyipa

3 Iwo amanola malilime awo kukhala akuthwa ngati a njoka;

4 Tetezeni Inu Yehova, kwa anthu oyipa;

5 Anthu odzikuza anditchera msampha mobisika;

6 Inu Yehova, ine ndikuti, “Ndinu Mulungu wanga.”

7 Inu Ambuye Wamphamvuzonse, Mpulumutsi wanga wamphamvu,

8 Musawapatse anthu oyipa zokhumba zawo, Inu Yehova;

9 Mitu ya amene andizungulira

10 Makala amoto agwere pa iwo;

11 Musalole kuti anthu achipongwe akhazikike mʼdziko;

12 Ndikudziwa kuti Yehova amapereka chiweruzo cholungama kwa anthu osauka,

13 Zoonadi anthu olungama adzatamanda dzina lanu,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado