1 Landitseni Yehova kwa anthu oyipa;
2 amene mu mtima mwawo amakonza zinthu zoyipa
3 Iwo amanola malilime awo kukhala akuthwa ngati a njoka;
4 Tetezeni Inu Yehova, kwa anthu oyipa;
5 Anthu odzikuza anditchera msampha mobisika;
6 Inu Yehova, ine ndikuti, “Ndinu Mulungu wanga.”
7 Inu Ambuye Wamphamvuzonse, Mpulumutsi wanga wamphamvu,
8 Musawapatse anthu oyipa zokhumba zawo, Inu Yehova;
9 Mitu ya amene andizungulira
10 Makala amoto agwere pa iwo;
11 Musalole kuti anthu achipongwe akhazikike mʼdziko;
12 Ndikudziwa kuti Yehova amapereka chiweruzo cholungama kwa anthu osauka,
13 Zoonadi anthu olungama adzatamanda dzina lanu,