Salmos 139

NYA

1 Inu Yehova, mwandisanthula

2 Inu mumadziwa pamene ndikhala pansi ndi pamene ndidzuka;

3 Mumapenyetsetsa pamene ndikutuluka ndi kugona kwanga;

4 Mawu asanatuluke pa lilime langa

5 Mumandizinga kumbuyo ndi kutsogolo komwe;

6 Nzeru zimenezi ndi zopitirira nzeru zanga,

7 Kodi ndingapite kuti kufuna kuzemba Mzimu wanu?

8 Ndikakwera kumwamba, Inu muli komweko;

9 Ngati ndiwulukira kotulukira dzuwa,

10 kumenekonso dzanja lanu lidzanditsogolera,

11 Ndikanena kuti, “Zoonadi, mdima udzandibisa ndithu

12 komabe mdimawo sudzakhala mdima kwa Inu;

13 Pakuti Inu munalenga za mʼkati mwanga;

14 Ndimakuyamikani chifukwa ndinapangidwa mochititsa mantha ndi modabwitsa;

15 Mapangidwe anga sanabisike pamaso panu

16 Maso anu anaona thupi langa lisanawumbidwe.

17 Zolingalira zanu pa ine ndi zamtengowapatali, Inu Mulungu,

18 Ndikanaziwerenga,

19 Ndi bwino mukanangopha anthu oyipa, Inu Mulungu!

20 Amayankhula za Inu ndi zolinga zoyipa;

21 Kodi ine sindidana nawo amene amakudani, Inu Yehova?

22 Ndimadana nawo kwathunthu;

23 Santhuleni, Inu Mulungu ndipo mudziwe mtima wanga;

24 Onani ngati muli mayendedwe aliwonse oyipa mwa ine,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado