Salmos 138

NYA

1 Ndidzakuyamikani Yehova ndi mtima wanga wonse;

2 Ndidzagwada kuyangʼana ku Nyumba yanu yoyera

3 Pamene ndinayitana, munandiyankha;

4 Mafumu onse a dziko lapansi akuyamikeni Yehova,

5 Iwo ayimbe za njira za Yehova,

6 Ngakhale kuti Yehova ngokwezeka, amasamalira odzichepetsa,

7 Ngakhale ndiyende pakati pa masautso,

8 Yehova adzakwaniritsa cholinga chake pa ine;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado