1 Ndidzakuyamikani Yehova ndi mtima wanga wonse;
2 Ndidzagwada kuyangʼana ku Nyumba yanu yoyera
3 Pamene ndinayitana, munandiyankha;
4 Mafumu onse a dziko lapansi akuyamikeni Yehova,
5 Iwo ayimbe za njira za Yehova,
6 Ngakhale kuti Yehova ngokwezeka, amasamalira odzichepetsa,
7 Ngakhale ndiyende pakati pa masautso,
8 Yehova adzakwaniritsa cholinga chake pa ine;