1 Mʼmbali mwa mitsinje ya ku Babuloni tinakhala pansi ndi kulira
2 Kumeneko, pa mitengo ya misondozi
3 pakuti anthu otigwira ukapolo anatipempha kuti tiyimbe nyimbo.
4 Tingayimbe bwanji nyimbo za Yehova
5 Ndikakuyiwala iwe Yerusalemu,
6 Lilime langa limamatire ku nkhama za mʼkamwa mwanga
7 Kumbukirani, Inu Yehova, zimene Aedomu anachita
8 Iwe mwana wa mkazi wa Babuloni, woyenera kuwonongedwa,
9 Amene adzagwira makanda ako