Salmos 137

NYA

1 Mʼmbali mwa mitsinje ya ku Babuloni tinakhala pansi ndi kulira

2 Kumeneko, pa mitengo ya misondozi

3 pakuti anthu otigwira ukapolo anatipempha kuti tiyimbe nyimbo.

4 Tingayimbe bwanji nyimbo za Yehova

5 Ndikakuyiwala iwe Yerusalemu,

6 Lilime langa limamatire ku nkhama za mʼkamwa mwanga

7 Kumbukirani, Inu Yehova, zimene Aedomu anachita

8 Iwe mwana wa mkazi wa Babuloni, woyenera kuwonongedwa,

9 Amene adzagwira makanda ako

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado