1 Ndinakondwera atandiwuza kuti,
2 Mapazi athu akuyima mʼzipata
3 Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda
4 Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko,
5 Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo,
6 Pemphererani mtendere wa Yerusalemu:
7 Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako,
8 Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga
9 Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu,